Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mbiri 12:13 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Nadzilimbitsa Rehabiamu mfumu m'Yerusalemu, nacita ufumu; pakuti Rehabiamu anali wa zaka makumi anai mphambu cimodzi polowa ufumu wace, nakhala mfumu zaka khumi ndi zisanu ndi ziwiri m'Yerusalemu, ndiwo mudzi Yehova adausankha m'mafuko onse a Israyeli, kuikapo dzina lace; ndipo dzina la mace ndiye Naama M-amoni.

Werengani mutu wathunthu 2 Mbiri 12

Onani 2 Mbiri 12:13 nkhani