Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mbiri 10:6 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Rehabiamu mfumu anafunsana ndi akulu akulu, amene anaimirira pamaso pa Solomo atate wace akali ndi moyo, nati, Mundipangire bwanji, kuti ndiwabwezere mau anthu awa?

Werengani mutu wathunthu 2 Mbiri 10

Onani 2 Mbiri 10:6 nkhani