Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mbiri 10:2 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo kunali, atamva Yerobiamu mwana wa Nebati (popeza anali m'Aigupto kumene adathawira, kuthawa Solomo mfumu), Yerobiamu anabwera kucoka ku Aigupto.

Werengani mutu wathunthu 2 Mbiri 10

Onani 2 Mbiri 10:2 nkhani