Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mafumu 8:3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo pakutha pace pa zaka zisanu ndi ziwirizo, mkaziyo anabwera kucoka m'dziko la Afilisti, naturuka kukanena za nyumba yace ndi munda wace kwa mfumu.

Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 8

Onani 2 Mafumu 8:3 nkhani