Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mafumu 7:16 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Naturuka anthu, nafunkha m'misasa ya Aaramu. Ndipo anagula miyeso wa ufa ndi sekeli, nagulanso miyeso iwiri ya barele ndi sekeli, monga umo adanenera Yehova.

Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 7

Onani 2 Mafumu 7:16 nkhani