Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mafumu 7:1 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Elisa anati, Mverani mau; a Yehova; atero Yehova, Mawa dzuwa lino adzagula muyeso wa ufa ndi sekeli, adzagulanso miyeso iwiri ya barele ndi sekeli, pa cipata ca Samariya.

Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 7

Onani 2 Mafumu 7:1 nkhani