Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mafumu 6:20 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo kunali, pakufika ku Samariya, Elisa anati, Yehova, muwakanganulire awa maso kuti aone. Nawakanganulira Yehova maso ao, naona iwo, ndipo tapenyani, ali pakati pa Samariya.

Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 6

Onani 2 Mafumu 6:20 nkhani