Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mafumu 25:13 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo zoimiritsa zamkuwa zinali m'nyumba ya Yehova, ndi maphaka ace, ndi thawale lamkuwa, zinali m'nyumba ya Yehova, Akasidi anazithyolathyola, natenga mkuwa wace kumka nao ku Babulo.

Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 25

Onani 2 Mafumu 25:13 nkhani