Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mafumu 24:4 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

ndiponso cifukwa ca mwazi wosacimwa adaukhetsa; popeza anadzaza Yerusalemu ndi mwazi wosacimwa; ndipo Yehova sanafuna kukhululukira.

Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 24

Onani 2 Mafumu 24:4 nkhani