Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mafumu 23:31 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Yoahazi anali wa zaka makumi awiri mphambu zitatu polowa ufumu wace, nakhala mfumu miyezi itatu m'Yerusalemu ndi dzina la mace ndiye Hamutali mwana wa Yeremiya wa ku Libina.

Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 23

Onani 2 Mafumu 23:31 nkhani