Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mafumu 22:9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Safani mlembiyo anadza kwa mfumu, nambwezera mfumu mau, nati, Anyamata anu anakhuthula ndalama zopereka m'nyumba, nazipereka m'dzanja la anchito akuyang'anira nyumba ya Yehova.

Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 22

Onani 2 Mafumu 22:9 nkhani