Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mafumu 19:9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anamva za Tirihaka mfumu ya Kusi, akuti, Taonani, waturuka kuthirana nawe nkhondo. Pamenepo anatumizanso mithenga kwa Hezekiya, ndi kuti,

Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 19

Onani 2 Mafumu 19:9 nkhani