Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mafumu 17:1 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Caka cakhumi ndi ziwiri ca Ahazi mfumu ya Yuda Hoseya mwana wa Ela analowa ufumu wace wa Israyeli m'Samariya, nakhala mfumu zaka zisanu ndi zinai.

Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 17

Onani 2 Mafumu 17:1 nkhani