Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mafumu 16:17 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo mfumu Ahazi anadula matsekerezo a maphaka, nacotsa mbiya pamwamba pao, natsitsa thawale pamwamba pa ng'ombe zamkuwa ziri pansi pace, naziika pa ciunda camiyala.

Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 16

Onani 2 Mafumu 16:17 nkhani