Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mafumu 15:8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Caka ca makumi atatu mphambu zisanu ndi zitatu ca Azariya mfumu ya Yuda, Zekariya mwana wa Yerobiamu anakhala mfumu ya Israyeli m'Samariya miyezi isanu ndi umodzi.

Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 15

Onani 2 Mafumu 15:8 nkhani