Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mafumu 15:5 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Yehova anadwaza mfumu, nakhala iye wakhate mpaka tsiku la imfa yace, nakhala m'nyumba ya padera. Ndipo Yotamu mwana wa mfumu anayang'anira banja la mfumu, naweruza anthu a m'dziko.

Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 15

Onani 2 Mafumu 15:5 nkhani