Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mafumu 15:17 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Caka ca makumi atatu mphambu zisanu ndi zinai ca Azariya mfumu ya Yuda, Menahemu mwana wa Gadi analowa ufumu wace wa Israyeti, nakhala mfumu zaka khumi m'Samariya.

Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 15

Onani 2 Mafumu 15:17 nkhani