Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mafumu 15:13 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Salumu mwana wa Yabesi analowa ufumu wace caka ca makumi atatu mphambu zisanu ndi zinai ca Uziya mfumu ya Yuda, nakhala mfumu mwezi umodzi m'Samariya.

Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 15

Onani 2 Mafumu 15:13 nkhani