Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mafumu 14:23 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Caka cakhumi ndi zisanu ca Amaziya mwana wa Yoasi mfumu ya Yuda, Yerobiamu mwana wa Yoasi mfumu ya Israyeli analowa ufumu wace m'Samariya, nakhala mfumu zaka makumi anai mphambu cimodzi.

Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 14

Onani 2 Mafumu 14:23 nkhani