Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mafumu 14:19 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anamcitira ciwembu m'Yerusalemu, nathawira iye ku Lakisi; koma anatumiza akumtsata ku Lakisi, namupha komweko.

Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 14

Onani 2 Mafumu 14:19 nkhani