Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mafumu 14:13 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Yoasi mfumu ya Israyeli anagwira Amaziya mfumu ya Yuda, mwana wa Yoasi mwana wa Ahaziya, ku Betisemesi, nadza ku Yerusalemu, nagamula linga la Yerusalemu kuyambira cipata ca Efraimu kufikira cipata ca kungondya, mikono mazana anai.

Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 14

Onani 2 Mafumu 14:13 nkhani