Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mafumu 12:7 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pamenepo mfumu Yoasi anaitana Yehoyada wansembe, ndi ansembe ena, nanena nao, Mulekeranji kukonza mogamuka nyumba? Tsono musalandiranso ndarama kwa anzanu odziwana nao, kuziperekera mogamuka nyumba.

Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 12

Onani 2 Mafumu 12:7 nkhani