Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mafumu 10:21 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Yehu anatumiza kwa Aisrayeti onse, nadza otumikira Baala onse, wosatsala ndi mmodzi yense wosafika. Nalowa m'nyumba ya Baala; ndi nyumba ya Baala inadzala pha.

Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 10

Onani 2 Mafumu 10:21 nkhani