Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mafumu 10:13 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Yehu anakomana nao abale a Ahaziya mfumu ya Yuda, nati, Ndinu ayani? Nati iwo, Ife ndife abale a Ahaziya, tirikutsika kulankhulira ana a mfumu, ndi ana a nyumba yaikuru.

Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 10

Onani 2 Mafumu 10:13 nkhani