Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mafumu 10:10 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Dziwani tsono, kuti sikadzagwa pansi kanthu ka mau a Yehova, amene Yehova ananena za nyumba va Ahabu; pakuti Yehova wacita cimene adanena mwa mtumiki wace Eliya.

Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 10

Onani 2 Mafumu 10:10 nkhani