Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Samueli 8:8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Monga nchito zao zonse anazicita kuyambira tsiku lija ndinawaturutsa ku Aigupto, kufikira lero lino kuti anandisiya Ine, natumikira milungu yina, momwemo alikutero ndi iwenso.

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 8

Onani 1 Samueli 8:8 nkhani