Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Samueli 7:16-17 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

16. Ndipo anayenda cozungulira caka ndi caka ku Beteli, ndi ku Giligala, ndi ku Mizipa; naweruza Israyeli m'malo onse amenewa.

17. Ndipo anabwera ku Rama, pakuti nyumba yace inali kumeneko; ndipo pamenepo anaweruza Israyeli; namangapo guwa la nsembe la Yehova.

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 7