Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Samueli 6:3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo iwo anati, Ngati mulitumiza kwina likasa la Mulungu wa Israyeli, musalitumize lopanda kanthu; koma makamaka mulibweze ndi nsembe yoparamula, mukatero mudzaciritsidwa, ndi kudziwa cifukwa cace dzanja lace liri pa inu losacoka.

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 6

Onani 1 Samueli 6:3 nkhani