Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Samueli 6:12 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo ng'ombezo zinatsata njira yolunjika ku Betisemesi, niziyenda mumseu, zirikulira poyenda; sizinapambukira ku dzanja lamanja, kapena kulamanzere; ndipo mafumu a Afilisti anazitsatira kufikira ku malire a Betisemesi.

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 6

Onani 1 Samueli 6:12 nkhani