Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Samueli 30:24 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo ndani adzabvomerezana nanu mrandu uwu? Pakuti monga gawo lace la iye wakumuka kunkhondoko, momwemo lidzakhala gawo lace la iye wakukhala ndi akatundu, adzagawana cimodzimodzi.

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 30

Onani 1 Samueli 30:24 nkhani