Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Samueli 27:2 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Davide ananyamuka, naoloka pamodzi ndi anthu mazana asanu ndi limodzi amene anali naye, nafika kwa Akisi mwana wa Maoki, mfumu ya ku Gati.

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 27

Onani 1 Samueli 27:2 nkhani