Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Samueli 26:23 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Yehova adzabwezera munthu yense cilungamo cace ndi cikhulupiriko cace, popeza Yehova anakuperekani lero m'dzanja langa, koma sindinalola kutukulira dzanja langa pa wodzozedwa wa Yehova,

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 26

Onani 1 Samueli 26:23 nkhani