Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Samueli 25:41 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo iye ananyamuka, nawerama nkhope yace pansi, nati, Onani, mdzakazi wanu ali kapolo wakusambitsa mapazi a anyamata a mbuye wanga.

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 25

Onani 1 Samueli 25:41 nkhani