Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Samueli 25:39 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo pamene Davide anamva kuti Nabala adamwalira, iye anati, Alemekezedwe Yehova, amene anaweruza mrandu wa mtonzo wanga wocokera ku dzanja la Nabala, naletsa mnyamata wace pa coipa; ndipo Yehova anabwezera pamutu pa Nabala coipa cace. Ndipo Davide anatumiza wokamfunsira Abigayeli, zakuti amtengere akhale mkazi wace.

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 25

Onani 1 Samueli 25:39 nkhani