Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Samueli 22:11 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pamenepo mfumu anatuma mthenga kukaitana Ahimeleki wansembeyo, mwana wa Ahitubu, ndi banja lonse la atate wace, ansembe a ku Nobi; ndipo iwo onse anafika kwa mfumu.

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 22

Onani 1 Samueli 22:11 nkhani