Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Samueli 21:6 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Comweco wansembeyo anampatsa mkate wopatulika, popeza panalibe mkate wina, koma mkate woonekera, umene adaucotsa pamaso pa Yehova, kuti akaike mkate wotentha tsiku lomwelo anacotsa winawo.

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 21

Onani 1 Samueli 21:6 nkhani