Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Samueli 20:34 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pamenepo Jonatani anauka pagome wolunda ndithu, osadya kanthu tsiku laciwiri la mwezi, pakuti mtima wace unali ndi cisoni cifukwa ca Davide, popeza atate wace anamcititsa manyazi.

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 20

Onani 1 Samueli 20:34 nkhani