Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Samueli 2:8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Amuutsa waumphawi m'pfumbi,Nanyamula wosowa padzala,Kukamkhalitsa kwa akalonga;Ndi kuti akhale naco colowa ca cimpando ca ulemerero;Cifukwa nsanamira za dziko lapansi nza Yehova,Ndipo iye anakhazika dziko pa izo,

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 2

Onani 1 Samueli 2:8 nkhani