Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Samueli 18:21 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Nati Sauli, Ndidzampatsa iye, kuti amkhalire msampha, ndi kuti dzanja la Afilisti limgwere. Cifukwa cace Sauli ananena ndi Davide, Lero udzakhala mkamwini wanga kaciwiri.

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 18

Onani 1 Samueli 18:21 nkhani