Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Samueli 17:4 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo ku zithando za Afilisti kunaturuka ciwinda, dzina lace Goliate wa ku Gati, kutalika kwace ndiko mikono isanu ndi umodzi ndi cikhato.

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 17

Onani 1 Samueli 17:4 nkhani