Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Samueli 17:23 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo m'mene iye anali cilankhulire nao, onani cinakwerako ciwindaco, Mfilisti wa ku Gati, dzina lace ndiye Goliate, woturuka pakati pa mipambo ya Afilisti, nalankhula monga mau omwe aja; ndipo Davide anawamva.

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 17

Onani 1 Samueli 17:23 nkhani