Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Samueli 17:12 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Tsono Davide anali mwana wa M-efrati uja wa ku Betelehemu-Yuda, dzina lace ndiye Jese; ameneyu anali nao ana amuna asanu ndi atatu; ndipo m'masiku a Sauli munthuyo anali nkhalamba, mwa anthu.

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 17

Onani 1 Samueli 17:12 nkhani