Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Samueli 14:36 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Sauli anati, Tiyeni titsikire usiku kwa Afilistiwo, ndi kuwawawanya kufikira kutayera, tisasiye munthu mmodzi wa iwowa. Ndipo iwo anati, Citani ciri conse cikukomerani. Pamenepo wansembeyo anati, Tisendere kwa Yehova kuno.

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 14

Onani 1 Samueli 14:36 nkhani