Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Samueli 14:14 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Kuwapha koyambako, Jonatani ndi wonyamula zida zace, anapha monga anthu makumi awiri, monga ndime ya munda yolima ng'ombe ziwiri tsiku limodzi.

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 14

Onani 1 Samueli 14:14 nkhani