Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Samueli 12:8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pamene Yakobo anafika ku Aigupto, ndi makolo anu anapemphera kwa Yehova, Yehova anatumiza Mose ndi Aroni, amene anaturutsa makolo anu m'Aigupto, nawakhalitsa pamalo pano,

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 12

Onani 1 Samueli 12:8 nkhani