Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Samueli 11:9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anati kwa mithenga inadzayi, Muzitero kwa anthu a ku Yabezi Gileadi, Mawa litatentha dzuwa, mudzaona cipulumutso. Ndipo mithenga inadza niuza a ku Yabezi; nakondwara iwowa.

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 11

Onani 1 Samueli 11:9 nkhani