Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Samueli 11:7 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Natenga ng'ombe ziwiri nazidula nthuli nthuli, nazitumiza m'malire monse mwa Israyeli, ndi dzanja la mithenga, nati, Amene sakudza pambuyo pa Sauli ndi pa Samueli, adzatero nazo ng'ombe zace. Ndipo kuopsa kwa Yehova kunawagwera anthu, naturuka ngati munthu mmodzi.

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 11

Onani 1 Samueli 11:7 nkhani