Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Samueli 10:24 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Samueli ananena ndi anthu onse, Mumuona kodi iye amene Yehova anamsankha, kuti palibe wina wakufanana naye pakati pa anthu onse? Ndipo anthu onse anapfuula, kuti, Akhale ndi moyo mfumuyo.

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 10

Onani 1 Samueli 10:24 nkhani