Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Samueli 1:8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo mwamuna wace Elikana anati kwa iye, Hana, umaliriranji? ndipo umakaniranji kudya? ndipo mtima wako uwawa ninji? Ine sindiri wakuposa ana khumi kwa iwe kodi?

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 1

Onani 1 Samueli 1:8 nkhani