Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mbiri 3:8-20 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

8. ndi Elisama, ndi Eliada, ndi Elifeleti, asanu ndi anai.

9. Onsewa ndiwo ana a Davide, pamodzi ndi ana a akazi ang'ono; ndipo Tamara ndiye mlongo wao.

10. Ndipo mwana wa Solomo ndiye Rehabiamu, Abiya mwana wace, Asa mwana wace, Yeo hosafati mwana wace,

11. Yoramu mwana wace, Ahaziya mwana wace, Yoasi mwana wace,

12. Amaziya mwana wace, Azariya mwana wace, Yotamu mwana wace,

13. Ahazi mwana wace, Hezekiya mwana wace, Manase mwana wace,

14. Amoni mwana wace, Yosiya mwana wace.

15. Ndi ana a Yosiya: woyamba Yohanana, waciwiri Yehoyakimu, wacitatu Zedekiya, wacinai Salumu.

16. Ndi ana a Yehoyakimu: Yekoniya mwana wace, Zedekiya mwana wace.

17. Ndi mwana wa Yekoniya: Asiri, Sealitiyeli mwana wace,

18. ndi Malikiramu, ndi Pedaya, ndi Senazara, Yekamiya, Hosama, Nedabiya.

19. Ndi ana a Pedaya: Zerubabeli, ndi Simei; ndi ana a Zerubabeli: Mesulamu, ndi Hananiya; ndipo Selomiti ndiye mlongo wao,

20. ndi Hasuba, ndi Oheli, ndi Berekiya, ndi Hasadiya, ndi Yusabi-hesedi; asanu.

Werengani mutu wathunthu 1 Mbiri 3